Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mbiri 5:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo zinatalikitsa mphikozo, kuti nsonga za mphiko zidaoneka kulikasa chakuno cha chipinda chamkati, koma sizinaoneke kubwalo; ndipo zili komweko mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo zinatalikitsa mphikozo, kuti nsonga za mphiko zidaoneka kulikasa chakuno cha chipinda chamkati, koma sizinaoneka kubwalo; ndipo zili komweko mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Mphikozo zinali zazitali kwambiri, kotero kuti nsonga zake zinkaonekera kukhalira ku malo opatulika kopambana patsogolo pa malo opatulika am'kati mwenimweni. Koma kunja sizinkaonekera. Ndipo zili komweko mpaka pano.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Mitengoyi inali yayitali kwambiri ndipo inkaonekera kunja kwa chipinda chamʼkati cha Malo Opatulika, koma osati kunja kwa Malo Opatulikawo; ndipo mitengoyi ilipo mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani




2 Mbiri 5:9
2 Mawu Ofanana  

Pakuti akerubi anafunyulula mapiko ao pamalo a likasa, ndi akerubi anaphimba likasa ndi mphiko zake pamwamba pake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa