Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 28:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo iwo analandira ndalamazo, nachita monga anawalangiza: ndipo mbiri iyo inabuka mwa Ayuda, kufikira lero lomwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo iwo analandira ndalamazo, nachita monga anawalangiza: ndipo mbiri iyo inabuka mwa Ayuda, kufikira lero lomwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Alonda aja atalandira ndalama zija, adachitadi monga momwe adaaŵauzira. Motero mbiri imeneyi idawanda pakati pa Ayuda mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Pamenepo alondawo anatenga ndalamazo nachita monga mmene anawuzidwira. Ndipo mbiri iyi inawanda pakati pa Ayuda mpaka lero lino.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 28:15
5 Mawu Ofanana  

nati, Mufuna kundipatsa chiyani, ndipo ine ndidzampereka Iye kwa inu? Ndipo iwo anamwerengera iye ndalama zasiliva makumi atatu.


Chifukwa chake munda umenewu anautcha, Munda-wa-mwazi, kufikira lero lino.


Koma iwo anatulukamo, nabukitsa mbiri yake m'dziko lonselo.


Koma iye anatuluka nayamba kulalikira ndithu, ndi kubukitsa mauwo, kotero kuti Yesu sanathe kulowanso poyera m'mudzi, koma anakhala padera m'mapululu; ndipo anadza kwa Iye anthu a kumalo onse.


Pakuti muzu wa zoipa zonse ndiwo chikondi cha pa ndalama; chimene ena pochikhumba, anasochera, nataya chikhulupiriro, nadzipyoza ndi zowawa zambiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa