Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 83:1 - Buku Lopatulika

Mulungu musakhale chete; musakhale duu, osanena kanthu, Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mulungu musakhale chete; musakhale duu, osanena kanthu, Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Mulungu, musakhalenso chete. Musangoti phee, musangoti duu, Inu Mulungu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu Mulungu musakhale chete; musangoti phee, Mulungu musangoti duu.

Onani mutuwo



Masalimo 83:1
7 Mawu Ofanana  

Kwa Inu, Yehova, ndidzafuulira; thanthwe langa, musandikhalire ngati wosamva; pakuti ngati munditontholera ine, ndidzafanana nao iwo akutsikira kumanda.


Yehova, mudazipenya; musakhale chete, Ambuye, musakhale kutali ndi ine.


Galamukani, mugoneranji, Ambuye? Ukani, musatitaye chitayire.


Mulungu wa milungu, Yehova, wanena, aitana dziko lapansi kuyambira kutuluka kwa dzuwa kufikira kulowa kwake.


Adzafika Mulungu wathu, ndipo sadzakhala chete. Moto udzanyeka pankhope pake, ndipo pozungulira pake padzasokosera kwakukulu.


Ndakhala nthawi yambiri wosalankhula ndakhala chete kudzithungata ndekha; tsopano ndidzafuula ngati mkazi wobala; ndidzapuma modukizadukiza ndi wefuwefu pamodzi.