Masalimo 82:8 - Buku Lopatulika8 Ukani, Mulungu, weruzani dziko lapansi; pakuti Inu mudzalandira amitundu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ukani, Mulungu, weruzani dziko lapansi; pakuti Inu mudzalandira amitundu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Dzambatukani, Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, popeza kuti mitundu yonse ya anthu ndi yanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu. Onani mutuwo |