Masalimo 44:23 - Buku Lopatulika23 Galamukani, mugoneranji, Ambuye? Ukani, musatitaye chitayire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Galamukani, mugoneranji, Ambuye? Ukani, musatitaye chitayire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Dzukani, Inu Ambuye. Chifukwa chiyani mukukhala ngati mwagona? Khalani maso, musatitaye kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Dzukani Ambuye! Nʼchifukwa chiyani mukugona! Dziwutseni nokha! Musatikane kwamuyaya. Onani mutuwo |