Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 82:7 - Buku Lopatulika

Komatu mudzafa monga anthu, ndipo mudzagwa monga wina wa akulu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Komatu mudzafa monga anthu, ndipo mudzagwa monga wina wa akulu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe mudzafa ngati anthu onse, ndipo mudzagwa ngati kalonga wina aliyense.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”

Onani mutuwo



Masalimo 82:7
5 Mawu Ofanana  

Potsiriza pake adzapita naye kumanda, nadzadikira pamanda pake.


Koma munthu wa ulemu wake sakhalitsa, afanana ndi nyama zakuthengo, afanana nazo.


Muwaike akulu ao ngati Orebu ndi Zeebu; mafumu ao ngati Zeba ndi Zalimuna,


Kodi udzanena ndithu pamaso pa iye wakupha iwe, Ine ndine Mulungu, pokhala uli munthu, wosati Mulungu, m'dzanja la iye wakupha iwe.


kuti mitengo iliyonse ya kumadzi isadzikuze chifukwa cha msinkhu wao, kapena kufikitsa nsonga zao pakati pa mitambo, ndi kuti amphamvu ao asaime m'kukula kwao, ndiwo onse akumwa madzi; pakuti onsewo aperekedwa kuimfa munsi mwake mwa dziko, pakati pa ana a anthu, pamodzi ndi iwo otsikira kumanda.