Masalimo 49:12 - Buku Lopatulika12 Koma munthu wa ulemu wake sakhalitsa, afanana ndi nyama zakuthengo, afanana nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma munthu wa ulemu wake sakhalitsa, afanana ndi nyama za kuthengo, afanana nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ngakhale munthu akhale wolemera chotani, komabe adzafa chabe ngati nyama zakuthengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ngakhale munthu akhale wachuma chotani, adzafa ngati nyama. Onani mutuwo |