Masalimo 49:11 - Buku Lopatulika11 Mumtima mwao ayesa kuti nyumba zao zikhala chikhalire, ndi mokhala iwo ku mibadwomibadwo; atchapo dzina lao padziko pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mumtima mwao ayesa kuti nyumba zao zikhala chikhalire, ndi mokhala iwo ku mibadwomibadwo; atchapo dzina lao padziko pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Manda ao ndiye kwao mpaka muyaya, ndi malo odzakhalako pa mibadwo yonse, ngakhale akadali moyo ankatcha maiko maina ao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Manda awo adzakhala nyumba zawo mpaka muyaya, malo awo okhalako kwa nthawi yonse ya mibado yawo, ngakhale anatchula malo mayina awo. Onani mutuwo |