Masalimo 49:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti aona anzeru amafa, monga aonongekera wopusa, wodyerera momwemo, nasiyira ena chuma chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti aona anzeru amafa, monga aonongekera wopusa, wodyerera momwemo, nasiyira ena chuma chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Zoonadi, aliyense atha kuwona kuti ngakhale anthu anzeru amafa. Chimodzimodzi, anthu opusa ndi opulukira ayenera kufa ndi kusiyira ena chuma chao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pakuti onse amaona kuti anthu anzeru amamwalira; opusa ndi opanda nzeru chimodzimodzinso amawonongeka ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena. Onani mutuwo |