Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 82:6 - Buku Lopatulika

Ndinati Ine, Inu ndinu milungu, ndi ana a Wam'mwambamwamba nonsenu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinati Ine, Inu ndinu milungu, ndi ana a Wam'mwambamwamba nonsenu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ine ndikuti, “Inu ndinu milungu, nonsenu ndinu ana a Mulungu Wopambanazonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’

Onani mutuwo



Masalimo 82:6
4 Mawu Ofanana  

Mulungu aima mu msonkhano wa Mulungu, aweruza pakati pa milungu.


Usapeputsa oweruza, kapena kutemberera mkulu wa anthu a mtundu wako.


Mlandu uliwonse wa cholakwa, kunena za ng'ombe, za bulu, za nkhosa, za chovala, za kanthu kalikonse kotayika, munthu anenako kali kake; mlandu wa onse awiri ufike kwa oweruza; iye amene oweruza amtsutsa alipe chowirikiza kwa mnansi wake.