Masalimo 82:1 - Buku Lopatulika1 Mulungu aima mu msonkhano wa Mulungu, aweruza pakati pa milungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mulungu aima mu msonkhano wa Mulungu, aweruza pakati pa milungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Mulungu akutsogolera msonkhano wakumwamba. Akugamula mlandu milungu ya pansi pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.” Onani mutuwo |