Masalimo 81:16 - Buku Lopatulika16 Akadawadyetsa naye tirigu wokometsetsa, ndikadakukhutitsanso ndi uchi wa m'thanthwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Akadawadyetsa naye tirigu wokometsetsa, ndikadakukhutitsanso ndi uchi wa m'thanthwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndikadakudyetsani ndi ufa wosalala watirigu, ndipo ndikadakukhutitsani ndi uchi wam'thanthwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma inu mukanadyetsedwa tirigu wabwino kwambiri; ndikanakukhutitsani ndi uchi wochokera pa thanthwe.” Onani mutuwo |