Masalimo 81:15 - Buku Lopatulika15 Akumuda Yehova akadamgonjera mungakhale monyenga, koma nyengo yao ikadakhala yosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Akumuda Yehova akadamgonjera mungakhale monyenga, koma nyengo yao ikadakhala yosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Anthu amene amadana ndi Chauta, akadakhwinyata pamaso pake, ndipo tsoka lao likadakhala mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Iwo amene amadana ndi Yehova akanakhwinyata pamaso pake, ndipo chilango chawo chinakakhala mpaka kalekale. Onani mutuwo |