Masalimo 82:2 - Buku Lopatulika2 Mudzaweruza mosalunjika kufikira liti, ndi kusamalira nkhope ya oipa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Mudzaweruza mosalunjika kufikira liti, ndi kusamalira nkhope ya oipa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Akuti, “Mudzakhalabe mukuweruza mopanda chilungamo mpaka liti? Bwanji mukupitirizabe kumakondera anthu oipa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa? Onani mutuwo |