Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 26:5 - Buku Lopatulika

Ndidana nao msonkhano wa ochimwa, ndipo sindidzakhala nao pansi ochita zoipa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndidana nao msonkhano wa ochimwa, ndipo sindidzakhala nao pansi ochita zoipa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndimadana ndi anthu ochita zoipa, sindikhala pamodzi ndi anthu oipa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa ndipo ndimakana kukhala pansi pamodzi ndi oyipa.

Onani mutuwo



Masalimo 26:5
6 Mawu Ofanana  

Wodala munthuyo wosayenda mu uphungu wa oipa, kapena wosaimirira m'njira ya ochimwa, kapena wosakhala pansi pa bwalo la onyoza.


Ndikwiya nao iwo akusamala zachabe zonama, koma ndikhulupirira Yehova.