Masalimo 31:6 - Buku Lopatulika6 Ndikwiya nao iwo akusamala zachabe zonama, koma ndikhulupirira Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndikwiya nao iwo akusamala zachabe zonama, koma ndikhulupirira Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Inu mumadana ndi opembedza mafano achabechabe. Koma ine ndimakhulupirira Inu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma ine ndimadana nawo amene amamamatira mafano achabechabe; ine ndimadalira Yehova. Onani mutuwo |