Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 148:1 - Buku Lopatulika

Aleluya. Lemekezani Yehova kochokera kumwamba; mlemekezeni m'misanje.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Aleluya. Lemekezani Yehova kochokera kumwamba; mlemekezeni m'misanje.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tamandani Chauta! Tamandani Chauta inu okhala kumwamba, mtamandeni inu okhala mu mlengalenga!

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tamandani Yehova. Tamandani Yehova, inu a kumwamba, mutamandeni Iye, inu a mlengalenga.

Onani mutuwo



Masalimo 148:1
8 Mawu Ofanana  

Lemekezani Yehova, inu, ntchito zake zonse, ponseponse pali ufumu wake: Lemekeza Yehova, moyo wanga iwe.


Aleluya; Ulemekeze Yehova, moyo wanga.


Zakumwamba ndi dziko lapansi zimlemekeze, nyanja ndi zonse zoyenda m'mwemo.


Ndipo kumwamba kudzalemekeza zodabwitsa zanu, Yehova; chikhulupiriko chanunso mu msonkhano wa oyera mtima.


Imbani inu, m'mwamba, nukondwere iwe dziko lapansi, imbani inu mapiri, pakuti Yehova watonthoza mtima wa anthu ake, nadzachitira chifundo ovutidwa ake.


Ndipo mipingo yakumtsogolera ndi yakumtsatira, inafuula, kuti, Hosana kwa Mwana wa Davide! Wolemekezeka ndiye wakudza m'dzina la Ambuye! Hosana mu Kumwambamwamba!