Masalimo 89:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo kumwamba kudzalemekeza zodabwitsa zanu, Yehova; chikhulupiriko chanunso mu msonkhano wa oyera mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo kumwamba kudzalemekeza zodabwitsa zanu, Yehova; chikhulupiriko chanunso mu msonkhano wa oyera mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Zakumwamba zimatamanda zodabwitsa zanu, Inu Chauta, zimatamanda kukhulupirika kwanu mu msonkhano wa oyera mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mayiko akumwamba amatamanda zozizwitsa zanu Yehova, kukhulupirika kwanunso, mu msonkhano wa oyera mtima anu. Onani mutuwo |