Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 140:8 - Buku Lopatulika

Yehova, musampatse woipa zokhumba iye; musamthandize zodzipanga zake; angadzikuze.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yehova, musampatse woipa zokhumba iye; musamthandize zodzipanga zake; angadzikuze.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu Chauta, musampatse munthu woipa zokhumba zake. Musathandizire chiwembu chake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova; musalole kuti zokonza zawo zitheke, mwina iwo adzayamba kunyada. Sela

Onani mutuwo



Masalimo 140:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo wina anauza Davide nati, Ahitofele ali pakati pa opangana chiwembu pamodzi ndi Abisalomu. Davide nati, Yehova, musandulize uphungu wa Ahitofele ukhale wopusa.


Ndiye amene apatsa mafumu chipulumutso: Amene alanditsa Davide mtumiki wake kulupanga loipa.


Musandipereke ku chifuniro cha akundisautsa, chifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zachiwawa.


Ndikadapanda kuopa mkwiyo wa pa mdani, angayese molakwa outsana nao, anganene, Lakwezeka dzanja lathu, ndipo Yehova sanachite ichi chonse.