Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 27:12 - Buku Lopatulika

12 Musandipereke ku chifuniro cha akundisautsa, chifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zachiwawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Musandipereke ku chifuniro cha akundisautsa, chifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zachiwawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Musandipereke m'manja mwa adani angawo. Mboni zonama zandiwukira, ndipo zimandiwopseza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Musandipereke ku zokhumba za adani anga, pakuti mboni zambiri zauka kutsutsana nane ndipo zikundiopseza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 27:12
17 Mawu Ofanana  

Yehova, musampatse woipa zokhumba iye; musamthandize zodzipanga zake; angadzikuze.


Penyani adani anga, popeza achuluka; ndipo andida ndi udani wachiwawa.


Ndipo simunandipereke m'dzanja la mdani; munapondetsa mapazi anga pali malo.


Mboni za chiwawa ziuka, zindifunsa zosadziwa ine.


Asanene mumtima mwao, Hede, momwemo! Asanene, Tammeza iye.


Pakuti ndinati, Asakondwerere ine; pakuterereka phazi langa, asadzikuze pa ine.


Umo ndidziwa kuti mukondwera ndi ine, popeza mdani wanga sandiseka.


Yehova adzamsunga, nadzamsunga ndi moyo, ndipo adzadalitsika padziko lapansi, ndipo musampereke ku chifuniro cha adani ake.


Usamnamizire mnzako.


Ndipo ndinawalanga kawirikawiri m'masunagoge onse, ndi kuwakakamiza anene zamwano; ndipo pakupsa mtima kwakukulu pa iwo ndinawalondalonda ndi kuwatsata ngakhale kufikira kumizinda yakunja.


Koma Saulo, wosaleka kupumira pa ophunzira a Ambuye kuopsa ndi kupha, ananka kwa mkulu wa ansembe,


Mboni yachiwawa ikaukira munthu kumneneza ndi kuti analakwa;


Chifukwa chake mbuye wanga mfumu amvere mau a kapolo wake. Ngati ndi Yehova anakuutsirani inu kutsutsana ndi ine, alandire chopereka; koma ngati ndi ana a anthu, atembereredwe pamaso pa Yehova, pakuti anandipirikitsa lero kuti ndisalandireko cholowa cha Yehova, ndi kuti, Muka, utumikire milungu ina.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa