Masalimo 27:13 - Buku Lopatulika13 Ndikadapanda kukhulupirira kuti ndikaone ubwino wa Yehova m'dziko la amoyo, ndikadatani! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndikadapanda kukhulupirira kuti ndikaone ubwino wa Yehova m'dziko la amoyo, ndikadatani! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndikhulupirira kuti ndidzaona ubwino wake wa Chauta m'dziko la amoyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi; ndidzaona ubwino wa Yehova mʼdziko la anthu amoyo. Onani mutuwo |