Masalimo 27:14 - Buku Lopatulika14 Yembekeza Yehova, limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako; inde, yembekeza Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Yembekeza Yehova, limbika, ndipo Iye adzalimbitsa mtima wako; inde, yembekeza Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Tsono khulupirira Chauta. Khala wamphamvu, ndipo ulimbe mtima. Ndithu, khulupirira Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Dikirani pa Yehova; khalani anyonga ndipo limbani mtima nimudikire Yehova. Onani mutuwo |