Masalimo 27:11 - Buku Lopatulika11 Mundiphunzitse njira yanu, Yehova, munditsogolere panjira yachidikha, chifukwa cha adani anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Mundiphunzitse njira yanu, Yehova, munditsogolere pa njira yachidikha, chifukwa cha adani anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mundiwonetse njira zanu zachifundo, Inu Chauta, munditsogolere m'njira yosalala, chifukwa ndili ndi adani ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Phunzitseni njira yanu Inu Yehova, munditsogolere mʼnjira yowongoka chifukwa cha ondizunza. Onani mutuwo |