Masalimo 144:10 - Buku Lopatulika10 Ndiye amene apatsa mafumu chipulumutso: Amene alanditsa Davide mtumiki wake kulupanga loipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndiye amene apatsa mafumu chipulumutso: Amene alanditsa Davide mtumiki wake kulupanga loipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Inu amene mumapambanitsa mafumu pankhondo, amene mumalanditsa Davide mtumiki wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 kwa Iye amene amapambanitsa mafumu, amene amapulumutsa Davide mtumiki wake ku lupanga loopsa. Onani mutuwo |