Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Masalimo 127:5 - Buku Lopatulika

Wodala munthu amene anadzaza nayo phodo lake: sadzachita manyazi iwo, pakulankhula nao adani kuchipata.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wodala munthu amene anadzaza nayo phodo lake: sadzachita manyazi iwo, pakulankhula nao adani kuchipata.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngwodala amene phodo lake nlodzaza ndi mivi yotere. Sadzamchititsa manyazi akamalankhula ndi adani ake pa bwalo lamilandu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.

Onani mutuwo



Masalimo 127:5
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yosefe anaona ana a Efuremu a mbadwo wachitatu; ananso a Makiri mwana wamwamuna wa Manase anabadwa pa maondo a Yosefe.


Ndipo anabala ana aamuna asanu ndi awiri, ndi ana aakazi atatu.


Ana ake akhala otekeseka, napsinjika kuchipata, wopanda wina wakuwapulumutsa.


Ndiye Mulungu amene andibwezerera chilango, nandigonjetsera mitundu ya anthu.


Mwananga, khala wanzeru, nukondweretse mtima wanga; kuti ndimuyankhe yemwe anditonza.