Masalimo 128:1 - Buku Lopatulika1 Wodala yense wakuopa Yehova, wakuyenda m'njira zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Wodala yense wakuopa Yehova, wakuyenda m'njira zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ngwodala aliyense woopa Chauta, amene amayenda m'njira zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Odala ndi onse amene amaopa Yehova, amene amayenda mʼnjira zake. Onani mutuwo |