Yobu 1:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anabala ana aamuna asanu ndi awiri, ndi ana aakazi atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anabala ana amuna asanu ndi awiri, ndi ana akazi atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anali ndi ana aamuna asanu ndi aŵiri, ndi ana aakazi atatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anali ndi ana aamuna asanu ndi awiri ndi ana aakazi atatu, Onani mutuwo |