Yobu 5:4 - Buku Lopatulika4 Ana ake akhala otekeseka, napsinjika kuchipata, wopanda wina wakuwapulumutsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ana ake akhala otekeseka, napsinjika kuchipata, wopanda wina wakuwapulumutsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ana ake alibe nchitetezo chomwe, amaŵapondereza m'bwalo lamilandu, palibe wina aliyense woŵapulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ana ake alibe ndi chitetezo chomwe; amaponderezedwa mʼbwalo la milandu popanda owateteza. Onani mutuwo |