Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 4:9 - Buku Lopatulika

Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu adati, “Yemwe ali ndi makutu akumva, amve!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo Yesu anati, “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”

Onani mutuwo



Marko 4:9
15 Mawu Ofanana  

Amene ali ndi makutu akumva, amve.


Amene ali ndi makutu, amve.


Ndipo Iye anaitana makamuwo nati kwa iwo, Imvani, nimudziwitse;


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


Mverani: taonani, wofesa anatuluka kukafesa;


Ndipo zina zinagwa m'nthaka yabwino, ndipo zinapatsa zipatso, ndi kukula ndi kuchuluka; ndipo zinabala kupindula makumi atatu, ndi makumi asanu ndi limodzi, ndi makumi khumi.


Chifukwa chake yang'anirani mamvedwe anu; pakuti kudzapatsidwa kwa iye amene ali nacho; ndipo kwa iye amene alibe chidzachotsedwa, chingakhale chija aoneka ngati ali nacho.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Iye amene apambana sadzachitidwa choipa ndi imfa yachiwiri.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye amene apambana ndidzampatsa kudya za ku mtengo wa moyo umene uli mu Paradaiso wa Mulungu.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.