Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 11:15 - Buku Lopatulika

15 Amene ali ndi makutu akumva, amve.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Amene ali ndi makutu akumva, amve.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Amene ali ndi makutu, amve!

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Iye amene ali ndi makutu amve.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 11:15
17 Mawu Ofanana  

Koma ndidzafanizira ndi chiyani obadwa awa a makono? Ali ofanana ndi ana akukhala m'mabwalo a malonda, amene alikuitana anzao.


Pomwepo olungamawo adzawalitsa monga dzuwa, mu Ufumu wa Atate wao. Amene ali ndi makutu amve.


Amene ali ndi makutu, amve.


Ngati munthu ali nao makutu akumva, amve.


Ndipo ananena, Amene ali nao makutu akumva amve.


kulibe kanthu kunja kwa munthu kukalowa mwa iye, kangathe kumdetsa: koma zinthu zakutuluka mwa munthu, ndizo zakumdetsa munthu.


Suyenera kuuthira pamunda kapena padzala, autaya kunja. Amene ali nao makutu akumva amve.


Ndipo zina zinagwa pa nthaka yokoma, ndipo zinamera, ndi kupatsa zipatso zamakumikhumi. Pakunena Iye izi anafuula, Iye amene ali ndi makutu akumva amve.


Ngati wina ali nalo khutu, amve.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Iye amene apambana sadzachitidwa choipa ndi imfa yachiwiri.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wopambana, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pamwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu aliyense koma iye wakuulandira.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wokhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye amene apambana ndidzampatsa kudya za ku mtengo wa moyo umene uli mu Paradaiso wa Mulungu.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Iye wakukhala nalo khutu amve chimene Mzimu anena kwa Mipingo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa