Mateyu 11:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ndipo ngati mukufunadi kukhulupirira zimenezi, Yohaneyo ndiye Eliya uja ankati adzabwerayu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo ngati inu mufuna kulandira izi, iyeyu ndi Eliya amene ankanena kuti adzabwera uja. Onani mutuwo |
Ndipo ndinaona mipando yachifumu, ndipo anakhala pamenepo; ndipo anawapatsa chiweruziro; ndipo ndinaona mizimu ya iwo amene adawadula khosi chifukwa cha umboni wa Yesu, ndi chifukwa cha mau a Mulungu, ndi iwo amene sanalambire chilombo, kapena fano lake, nisanalandire lembalo pamphumi ndi padzanja lao; ndipo anakhala ndi moyo, nachita ufumu pamodzi ndi Khristu zaka chikwi.