Mateyu 11:13 - Buku Lopatulika13 Pakuti aneneri onse ndi chilamulo chinanenera kufikira pa Yohane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pakuti aneneri onse ndi chilamulo chinanenera kufikira pa Yohane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Aneneri onse ndiponso Malamulo a Mose ankaneneratu za Ufumu umenewu mpaka nthaŵi ya Yohane Mbatizi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti aneneri onse ndi malamulo ananenera kufikira nthawi ya Yohane. Onani mutuwo |