Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 11:13 - Buku Lopatulika

13 Pakuti aneneri onse ndi chilamulo chinanenera kufikira pa Yohane.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Pakuti aneneri onse ndi chilamulo chinanenera kufikira pa Yohane.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Aneneri onse ndiponso Malamulo a Mose ankaneneratu za Ufumu umenewu mpaka nthaŵi ya Yohane Mbatizi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pakuti aneneri onse ndi malamulo ananenera kufikira nthawi ya Yohane.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 11:13
10 Mawu Ofanana  

Ndipo adzabwezera mitima ya atate kwa ana, ndi mitima ya ana kwa atate ao; kuti ndisafike ndi kukantha dziko lionongeke konse.


Ndipo kuyambira masiku a Yohane Mbatizi, kufikira tsopano lino, Ufumu wa Kumwamba uli wokakamizidwa, ndipo okakamirawo aukwatula ndi mphamvu.


Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.


Ndipo anayamba kwa Mose, ndi kwa aneneri onse nawatanthauzira iwo m'malembo onse zinthu za Iye yekha.


Ndipo anati kwa iwo, Awa ndi mauwo ndinalankhula nanu, paja ndinakhala ndi inu, kuti ziyenera kukwanitsidwa zonse zolembedwa za Ine m'chilamulo cha Mose, ndi aneneri, ndi Masalimo.


Pakuti iwo akukhala mu Yerusalemu, ndi akulu ao, popeza sanamzindikire Iye, ngakhale mau a aneneri owerengedwa masabata onse, anawakwaniritsa pakumtsutsa.


Koma tsopano chilungamo cha Mulungu chaoneka chopanda lamulo, chilamulo ndi aneneri achitira ichi umboni;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa