Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Marko 3:1 - Buku Lopatulika

Ndipo analowanso m'sunagoge; ndipo munali munthu m'menemo ali ndi dzanja lake lopuwala.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo analowanso m'sunagoge; ndipo munali munthu m'menemo ali ndi dzanja lake lopuwala.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yesu adakaloŵanso m'nyumba yamapemphero. M'menemo mudaali munthu wina wopuwala dzanja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi inanso analowa mʼsunagoge, ndipo munthu wa dzanja lolumala anali momwemo.

Onani mutuwo



Marko 3:1
7 Mawu Ofanana  

Ndipo kunachitika, pakumva mfumu mau a munthu wa Mulungu amene anawafuula, kutemberera guwa la nsembe mu Betele, Yerobowamu anatansa dzanja lake ali ku guwalo, nati, Mgwireni iye. Ndipo dzanja lake analitansira kwa iye linauma, kuti sanathe kulifunyatitsanso.


Ndipo iwo analowa mu Kapernao; ndipo pomwepo pa tsiku la Sabata iye analowa m'sunagoge naphunzitsa.


Ndipo analowa m'masunagoge mwao mu Galileya monse, nalalikira, natulutsa ziwanda.


motero Mwana wa Munthu ali mwini tsiku la Sabata lomwe.


M'menemo munagona khamu lalikulu la anthu odwala, akhungu, opunduka miyendo, opuwala.