Yohane 5:3 - Buku Lopatulika3 M'menemo munagona khamu lalikulu la anthu odwala, akhungu, opunduka miyendo, opuwala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 M'menemo munagona khamu lalikulu la anthu odwala, akhungu, opunduka miyendo, opuwala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 M'makondemo munkagona anthu ambiri odwala, akhungu, opunduka miyendo ndi opuwala ziwalo. [Iwoŵa ankadikira kuti madzi agwedezeke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Mʼmenemo munkagonamo gulu lalikulu la anthu odwala, osaona, olumala ndi ofa ziwalo. Onani mutuwo |