Yohane 5:5 - Buku Lopatulika5 Koma panali munthu wina apo, ali m'kudwala kwake zaka makumi atatu kudza zisanu ndi zitatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma panali munthu wina apo, ali m'kudwala kwake zaka makumi atatu kudza zisanu ndi zitatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pakati pa anthu odwalawo panali wina amene adaadwala zaka 38. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mmodzi wa amene anali pamenepo anali atadwala zaka 38. Onani mutuwo |