Yohane 5:2 - Buku Lopatulika2 Koma pali thamanda mu Yerusalemu pa Chipata cha Nkhosa, lotchedwa mu Chihebri Betesida, lili ndi makonde asanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma pali thamanda m'Yerusalemu pa Chipata cha Nkhosa, lotchedwa m'Chihebri Betesida, lili ndi makonde asanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Kumeneko kuli dziŵe, dzina lake pa Chiyuda ndi Betesida. Dziŵeli lili pafupi ndi Chipata cha Nkhosa, ndipo nlozingidwa ndi makonde asanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo ku Yerusalemuko pafupi ndi chipata cha Nkhosa kuli dziwe limene mʼChihebri limatchedwa Betisaida ndipo ndi lozunguliridwa ndi makumbi asanu. Onani mutuwo |