Marko 3:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anamuyang'anira Iye, ngati adzamchiritsa tsiku la Sabata; kuti ammange mlandu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anamuyang'anira Iye, ngati adzamchiritsa tsiku la Sabata; kuti ammange mlandu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Anthu ena ankafuna chifukwa choti akamnenezere Yesuyo, motero ankangomuyang'anitsitsa kuti aone ngati achiritse munthuyo pa tsiku la Sabata. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ena a iwo anafunafuna chifukwa chakuti akamuneneze Yesu, potero anamuyangʼanitsitsa kuti aone ngati angamuchiritse tsiku la Sabata. Onani mutuwo |