Marko 3:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo ananena ndi munthu ali ndi dzanja lopuwala, Taimirira pakati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo ananena ndi munthu ali ndi dzanja lopuwala, Taimirira pakati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yesu adalamula munthuyo kuti, “Imirira, bwera kutsogolo kuno.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Yesu anati kwa munthu wolumala dzanjayo, “Imirira, bwera kuno kutsogolo.” Onani mutuwo |