Marko 2:28 - Buku Lopatulika28 motero Mwana wa Munthu ali mwini tsiku la Sabata lomwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 motero Mwana wa Munthu ali mwini tsiku la Sabata lomwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Choncho Mwana wa Munthu ali ndi ulamuliro wonse pa zokhudza tsiku la Sabata.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Choncho Mwana wa Munthu ali Ambuye ngakhale wa Sabata.” Onani mutuwo |