Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 2:28 - Buku Lopatulika

28 motero Mwana wa Munthu ali mwini tsiku la Sabata lomwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 motero Mwana wa Munthu ali mwini tsiku la Sabata lomwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Choncho Mwana wa Munthu ali ndi ulamuliro wonse pa zokhudza tsiku la Sabata.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Choncho Mwana wa Munthu ali Ambuye ngakhale wa Sabata.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 2:28
13 Mawu Ofanana  

pakuti Mwana wa Munthu ali mwini tsiku la Sabata.


Ndipo ananena nao, Sabata linaikidwa chifukwa cha munthu, si munthu chifukwa cha Sabata;


Ndipo analowanso m'sunagoge; ndipo munali munthu m'menemo ali ndi dzanja lake lopuwala.


Ndipo ananena kwa iwo, Kodi nkuloledwa tsiku la Sabata kuchita zabwino, kapena zoipa? Kupulumutsa moyo kapena kupha? Koma anakhala chete.


Ndipo Iye ananena kwa iwo, kuti, Mwana wa Munthu ali Mbuye wa tsiku la Sabata.


Koma Yesu anayankha iwo, Atate wanga amagwira ntchito kufikira tsopano, Inenso ndigwira ntchito.


Koma tsikulo ndi la Sabata limene Yesu anakanda thope, namtsegulira iye maso ake.


Ena pamenepo mwa Afarisi ananena, Munthu uyu sachokera kwa Mulungu, chifukwa sasunga Sabata. Koma ena ananena, Munthu ali wochimwa akhoza bwanji kuchita zizindikiro zotere? Ndipo panali kutsutsana mwa iwo.


ndipo anakonza zonse pansi pa mapazi ake, nampatsa Iye akhale mutu pamutu pa zonse, kwa Mpingo


Ndinagwidwa ndi Mzimu tsiku la Ambuye, ndipo ndinamva kumbuyo kwanga mau aakulu, ngati a lipenga,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa