Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 5:9 - Buku Lopatulika

Pakuti chizizwo chidagwira iye, ndi onse amene anali naye, pa kusodzako kwa nsomba zimene anazikola;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti chizizwo chidagwira iye, ndi onse amene anali naye, pa kusodzako kwa nsomba zimene anazikola;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaatero popeza kuti iye, pamodzi ndi onse amene anali naye, adaazizwa nako kuchuluka kwa nsomba zimene adaaphazo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye ndi anzake onse anadabwa ndi nsomba zimene anagwira,

Onani mutuwo



Luka 5:9
8 Mawu Ofanana  

Munamchititsa ufumu pa ntchito za manja anu; mudagonjetsa zonse pansi pa mapazi ake;


mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja. Zopita m'njira za m'nyanja.


Pakuti sanadziwe chimene adzayankha; chifukwa anachita mantha ndithu.


Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.


chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro.


Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzake, nanena, Mau amenewa ali otani? Chifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingotuluka.


ndipo chimodzimodzinso Yakobo ndi Yohane, ana a Zebedeo, amene anali anzake a Simoni. Ndipo Yesu anati kwa Simoni, Usaope, kuyambira tsopano udzakhala msodzi wa anthu.


Koma Simoni Petro, pamene anaona, anagwa pansi pa mawondo ake a Yesu, nanena, Muchoke kwa ine, Ambuye, chifukwa ndine munthu wochimwa.