Masalimo 8:6 - Buku Lopatulika6 Munamchititsa ufumu pa ntchito za manja anu; mudagonjetsa zonse pansi pa mapazi ake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Munamchititsa ufumu pa ntchito za manja anu; mudagonjetsa zonse pansi pa mapazi ake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mudampatsa ulamuliro pa ntchito za manja anu. Mudamgonjetsera zolengedwa zonse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Inu munamuyika wolamulira ntchito ya manja anu; munayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake; Onani mutuwo |