Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 2:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Onse amene ankamva, ankadabwa ndi zimene abusawo ankaŵasimbira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 ndipo onse amene anamva zimene abusawa ananena anadabwa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 2:18
8 Mawu Ofanana  

Taonani, ine ndi ana amene Yehova wandipatsa ine, tili zizindikiro ndi zodabwitsa mwa Israele, kuchokera kwa Yehova wa makamu, amene akhala m'phiri la Ziyoni.


Ndipo iwo, m'mene anaona, anadziwitsa anthu za mau analankhulidwa kwa iwo a mwana uyu.


Koma Maria anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwake.


Ndipo atate ndi amake anali kuzizwa ndi zinthu zolankhulidwa za Iye.


Ndipo onse amene anamva Iye anadabwa ndi chidziwitso chake, ndi mayankho ake.


Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzake, nanena, Mau amenewa ali otani? Chifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingotuluka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa