Luka 2:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo anthu onse amene anamva anazizwa ndi zinthu abusa adalankhula nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Onse amene ankamva, ankadabwa ndi zimene abusawo ankaŵasimbira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 ndipo onse amene anamva zimene abusawa ananena anadabwa. Onani mutuwo |