Luka 2:19 - Buku Lopatulika19 Koma Maria anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Maria anasunga mau awa onse, nawalingalira mumtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma Maria adasunga zonsezo namazilingalira mumtima mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma Mariya anasunga zonsezi mu mtima mwake ndi kumazilingalira. Onani mutuwo |