Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 4:32 - Buku Lopatulika

32 chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Zophunzitsa zake anthu zidaaŵagwira mtima kwambiri, chifukwa ankalankhula moonetsa ulamuliro ngati mwiniwake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Iwo anadabwa ndi chiphunzitso chake chifukwa uthenga wake unali ndi ulamuliro.

Onani mutuwo Koperani




Luka 4:32
15 Mawu Ofanana  

Ndipo anazizwa ndi chiphunzitso chake; pakuti anaphunzitsa monga mwini mphamvu, si monga alembi.


Ndipo onse amene anamva Iye anadabwa ndi chidziwitso chake, ndi mayankho ake.


Ndipo m'sunagoge munali munthu, wokhala nacho chiwanda chonyansa; nafuula ndi mau olimba, kuti,


Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzake, nanena, Mau amenewa ali otani? Chifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingotuluka.


Wopatsa moyo ndi mzimu; thupi silithandiza konse. Mau amene ndalankhula ndi inu ndiwo mzimu, ndi moyo.


Anyamatawo anayankha, Nthawi yonse palibe munthu analankhula chotero.


koma takaniza zobisika za manyazi, osayendayenda mochenjerera, kapena kuchita nao mau a Mulungu konyenga; koma ndi maonekedwe a choonadi; tidzivomeretsa tokha ku chikumbumtima cha anthu onse pamaso pa Mulungu.


kuti Uthenga Wabwino wathu sunadze kwa inu m'mau mokha, komatunso mumphamvu, ndi mwa Mzimu Woyera, ndi m'kuchuluka kwakukulu; monga mudziwa tinakhala onga otani mwa inu chifukwa cha inu.


Izi lankhula, ndipo uchenjeze, nudzudzule ndi ulamuliro wonse. Munthu asakupeputse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa