Luka 4:32 - Buku Lopatulika32 chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 chifukwa mau ake anali ndi ulamuliro. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Zophunzitsa zake anthu zidaaŵagwira mtima kwambiri, chifukwa ankalankhula moonetsa ulamuliro ngati mwiniwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Iwo anadabwa ndi chiphunzitso chake chifukwa uthenga wake unali ndi ulamuliro. Onani mutuwo |