Luka 4:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo m'sunagoge munali munthu, wokhala nacho chiwanda chonyansa; nafuula ndi mau olimba, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo munali m'sunagoge munthu, wokhala nacho chiwanda chonyansa; nafuula ndi mau olimba, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 M'nyumba yamapempheroyo munali munthu wogwidwa ndi mzimu womuipitsa. Adalankhula mokuwa kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Mʼsunagogemo munali munthu wogwidwa ndi mzimu woyipa. Iye analira ndi mawu akulu, akuti Onani mutuwo |