Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 24:3 - Buku Lopatulika

Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaloŵa m'mandamo koma sadaupeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo atalowamo sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.

Onani mutuwo



Luka 24:3
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzira anadza kutsidya linalo, naiwala kutenga mikate.


Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda.


ndipo m'mene sanapeze mtembo wake, anadza, nanena kuti adaona m'masomphenya angelo, amene ananena kuti ali ndi moyo Iye.


Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire.


Potero kuyenera kuti wina wa amunawo anatsatana nafe nthawi yonseyi Ambuye Yesu analowa natuluka mwa ife,