Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Adapeza chimwala chija chili chogubuduza kale kuchoka pakhomo pa manda aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Anaona mwala wa pa manda utagubuduzika

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:2
9 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, panali chivomezi chachikulu; pakuti mngelo wa Ambuye anatsika Kumwamba, nafika kukunkhuniza mwalawo, nakhala pamwamba pake.


Koma tsiku loyamba la sabata, mbandakucha, anadza kumanda atatenga zonunkhira adazikonza.


Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.


Pamenepo Yesu, ndi kudzumanso mwa Iye yekha anadza kumanda. Koma panali phanga, ndipo mwala unaikidwa pamenepo.


Pomwepo anachotsa mwala. Koma Yesu anakweza maso ake kupenya kumwamba nati, Atate, ndiyamika Inu kuti munamva Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa