Luka 24:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anapeza mwala unakunkhunizidwa kuuchotsa pamanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adapeza chimwala chija chili chogubuduza kale kuchoka pakhomo pa manda aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anaona mwala wa pa manda utagubuduzika Onani mutuwo |