Mateyu 16:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ophunzira anadza kutsidya linalo, naiwala kutenga mikate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ophunzira anadza kutsidya linalo, naiwala kutenga mikate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pamene ophunzira aja adakafika kutsidya, anali ataiŵala kutenga buledi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma atawoloka nyanja, ophunzira anayiwala kutenga buledi. Onani mutuwo |