Luka 7:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo pamene Ambuye anamuona, anagwidwa ndi chifundo chifukwa cha iye, nanena naye, Usalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Pamene Ambuye adamuwona, adamumvera chisoni, namuuza kuti, “Mai, musalire.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ambuye atamuona mayiyo, mtima wawo unagwidwa naye chifundo ndipo anati, “Usalire.” Onani mutuwo |