Machitidwe a Atumwi 1:21 - Buku Lopatulika21 Potero kuyenera kuti wina wa amunawo anatsatana nafe nthawi yonseyi Ambuye Yesu analowa natuluka mwa ife, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Potero kuyenera kuti wina wa amunawo anatsatana nafe nthawi yonseyi Ambuye Yesu analowa natuluka mwa ife, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Pali anthu ena amene akhala akutsagana nafe nthaŵi yonse pamene Ambuye Yesu anali pakati pathu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Chifukwa chake ndi kofunika kusankha mmodzi wa anthu amene akhala nafe nthawi yonse imene Ambuye Yesu ankayenda nafe, Onani mutuwo |